lirik lagu mastol – anakonza
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-verse 1-
mtima w-nga unasweka zinatsala ndi zidutswa//
nde nkhani za chikondi ndimazileka zizidutsa//
sind-nkafuna olo k-mva n’nasanduka gonthi//
mu mtima munadzadza ndi milandu ngati khothi//
ena ankaunena mtima w-nga ati ndiwo-//
vuta kuwukonda mwina umafila aunt tiwo//
anzanga mmawashisha akafusa ngati ndiwo//
anapangitsa kuti ine ndizikhalabe single//
ntak-mana ndiwe dziko linayamba kuzuna//
anthu anadziwa mtumwi wapeza ka tsuna//
thupi losala-la ngati sadwala malungo//
she a catholic,mfana wa aroma moti nnafera fungo//
ndapezadi sindingachite makaniso//
mtimau mwatengadi sindingasinthe maganizo//
ndaona kuwala kwako nde ndavomereza sure//
olenga iwe -n-lengaso nyenyezi ndi dzuwa//
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-hook-
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
-verse 2-
anakonza inuyo mami eeh ndi kadaulo//
ntchito anayigwira palibe dandaulo//
monga khristu akondera church mmau a paulo//
nane nzakukonda choncho kukusiya ndi malaulo//
ndi kokongoletsa nde chikondi ndikatapila//
musandivuwule mtima mwake ndikakamila//
structure ya fine ngati clay soil//
kubhebha sikuchepa olo asinthe hairstyle//
mmmh beiby nzakutengera ku nkopola//
kukusintha dzina udzakhala mayi topola//
tiye kwanu konko tikalipire ya lobola//
kutsimikiza kuti palibe ozandisomphola//
ndili nawe plan ma//
ndikaona maso ake othwanima//
(maso akewo)
tsemwe ndikudziwa kuti yemwe//
-n-lenga nyenyezi -n-lenga ndiwe wemwe//
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-hook-
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
-bridge-
ine ndakonda iwe wekha//
kukusiya ndi zosatheka//
i swear there is n-body better//
yahweh anakonza iwe//
-pre-hook-
kuwala kwako ngakhale dzuwa limayimika manja//
n’naponda potani kuti iweyo ukhale w-nga//
-n-lenga nyenyezi ndi dzuwa,ndi amene -n-lenga iwe//
ndifunitsitsa tikathere pa guwa,mtima w-nga watenga ndiwe//
-hook-
na iwe anakonza beiby
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
na iwe anakonza
(na iwe anakonza)
s-n-lakwitse anakonza
(na iwe anakonza)
Lirik lagu lainnya:
- lirik lagu dr.fuchs – köle gibi
- lirik lagu justhis – jesus
- lirik lagu coldburn – bite the dust
- lirik lagu avatar darko – 2wo or thr33
- lirik lagu the reatards – you fucked up my dreams
- lirik lagu the hill country devil – rats get fat
- lirik lagu orchestral manoeuvres in the dark – don’t go
- lirik lagu luminary x m7 – nuke
- lirik lagu pro teens – timmy gun
- lirik lagu daesung – 世界が終わっても (even when the world ends)