
lirik lagu national anthem - malawi native anthem text
Loading...
1.
mlungu dalitsani malawi,
mumsunge m’mtendere.
gonjetsani adani onse,
njala, nthenda, nsanje.
lunzitsani mitima yathu,
kuti tisaope.
mdalitse mtsogo leri na fe,
ndi mai malawi.
2.
malawi ndziko lokongola,
la chonde ndi ufulu,
nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
ndithudi tadala.
zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
n’mphatso zaulere.
nkhalango, madambo abwino.
ngwokoma malawi.
3.
o! ufulu tigwirizane,
kukweza malawi.
ndi chikondi, khama, k-mvera,
timutumikire.
pa nkhondo nkana pa mtendere,
cholinga n’chimodzi.
mai, bambo, tidzipereke,
pokweza malawi.
sent by carlos andré pereira da silva branco
Lirik lagu lainnya:
- lirik lagu save the last dance - crazy(real)
- lirik lagu pedro the lion - beauty queens
- lirik lagu save the last dance - murder she wrote
- lirik lagu pedro the lion - breadwinner you
- lirik lagu pedro the lion - discretion
- lirik lagu pedro the lion - diamond ring
- lirik lagu save the last dance - only you ( bad boy remix)
- lirik lagu save the last dance - u know whats up
- lirik lagu nat king cole - funny
- lirik lagu nat king cole - don't blame me